Logoja YouVersion
Ikona e kërkimit

YOHANE 8:12

YOHANE 8:12 BLP-2018

Pamenepo Yesu analankhulanso nao, nanena, Ine ndine kuunika kwa dziko lapansi; iye wonditsata Ine sadzayenda mumdima, koma adzakhala nako kuunika kwa moyo.