1
YOHANE 13:34-35
Buku Lopatulika
Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake. Mwa ichi adzazindikira onse kuti muli ophunzira anga, ngati muli nacho chikondano wina ndi mnzake.
Krahaso
Eksploroni YOHANE 13:34-35
2
YOHANE 13:14-15
Chifukwa chake, ngati Ine Ambuye ndi Mphunzitsi, ndasambitsa mapazi anu, inunso muyenera kusambitsana mapazi wina ndi mnzake. Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite.
Eksploroni YOHANE 13:14-15
3
YOHANE 13:7
Yesu anayankha nati kwa iye, Chimene ndichita Ine suchidziwa tsopano; koma udzadziwa m'tsogolo mwake.
Eksploroni YOHANE 13:7
4
YOHANE 13:16
Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake; kapena mtumwi sali wamkulu ndi womtuma iye.
Eksploroni YOHANE 13:16
5
YOHANE 13:17
Ngati mudziwa izi, odala inu ngati muzichita.
Eksploroni YOHANE 13:17
6
YOHANE 13:4-5
ananyamuka pamgonero, navula malaya ake; ndipo m'mene adatenga chopukutira, anadzimanga m'chuuno. Pomwepo anathira madzi m'beseni, nayamba kusambitsa mapazi a ophunzira ake, ndi kuwapukuta ndi chopukutira, chimene anadzimanga nacho.
Eksploroni YOHANE 13:4-5
Kreu
Bibla
Plane
Video