Ntc. 4:13

Ntc. 4:13 BLY-DC

Abwalo aja adazizwa poona kulimba mtima kwa Petro ndi Yohane, ndiponso podziŵa kuti anali anthu wamba, osaphunzira kwambiri. Apo adazindikira kuti anali anzake a Yesu.

Read Ntc. 4

මෙයට අදාළ වීඩියෝ