1
Genesis 5:24
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Enoki anayenda ndi Mulungu; ndipo iye sanaonekenso chifukwa Mulungu anamutenga.
Compare
Genesis 5:24ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
2
Genesis 5:22
Atabadwa Metusela, Enoki anayenda ndi Mulungu zaka 300 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
Genesis 5:22ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
3
Genesis 5:1
Ndondomeko ya mibado ya Adamu ndi iyi: Pamene Mulungu analenga munthu, anamulenga mʼchifaniziro cha Mulungu.
Genesis 5:1ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
4
Genesis 5:2
Iye analenga mwamuna ndi mkazi. Anawadalitsa ndipo anawatcha “Munthu.”
Genesis 5:2ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
Home
ਬਾਈਬਲ
Plans
ਵੀਡੀਓ