GENESIS 4:15

GENESIS 4:15 BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.

Video for GENESIS 4:15

Gratis leseplaner og andakter relatert til GENESIS 4:15