YouVersion logo
BibelLeseplanerVideoer
Få appen
Språkvelger
Søkeikon

Populære bibelvers fra Gen. 2

1

Gen. 2:24

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.

Sammenlign

Utforsk Gen. 2:24

2

Gen. 2:18

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”

Sammenlign

Utforsk Gen. 2:18

3

Gen. 2:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.

Sammenlign

Utforsk Gen. 2:7

4

Gen. 2:23

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”

Sammenlign

Utforsk Gen. 2:23

5

Gen. 2:3

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.

Sammenlign

Utforsk Gen. 2:3

6

Gen. 2:25

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.

Sammenlign

Utforsk Gen. 2:25

Forrige kapittel
Neste kapittel
YouVersion

Oppmuntrer og utfordrer deg til å søke nærhet med Gud hver dag.

Tjeneste

Om

Karrierer

Frivillig

Blogg

Presse

Nyttige lenker

Hjelp

Gi

Bibeloversettelser

Lydbibler

Bibelspråk

Dagens bibelvers


En digital tjeneste av

Life.Church
Norsk

©2026 Life.Church / YouVersion

PersonvernerklæringVilkår
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest