1
Yoh. 7:38
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Paja Malembo akuti, ‘Munthu wokhulupirira Ine, mtima wake udzakhala ngati gwelo la mitsinje ya madzi opatsa moyo.’ ”
နှိုင်းယှဉ်
Yoh. 7:38ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
2
Yoh. 7:37
Tsiku lotsiriza la chikondwerero chija linali lalikulu. Pa tsikulo Yesu adaimirira nkunena mokweza kuti, “Ngati pali munthu ali ndi ludzu, abwere kwa Ine kuti adzamwe.
Yoh. 7:37ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
3
Yoh. 7:39
(Pakutero Yesu ankanena za Mzimu Woyera amene anthu okhulupirira Iye analikudzalandira. Nthaŵi imeneyo nkuti Mzimu Woyera asanafike, chifukwa Yesu anali asanalandire ulemerero wake.)
Yoh. 7:39ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
4
Yoh. 7:24
Musamaweruza poyang'ana maonekedwe chabe, koma muziweruza molungama.”
Yoh. 7:24ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
5
Yoh. 7:18
Amene amangolankhula zakezake, amadzifunira yekha ulemu. Koma yemwe amafunira ulemu amene adamtuma, ameneyo ndiye woona, ndipo mumtima mwake mulibe chinyengo.
Yoh. 7:18ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
6
Yoh. 7:16
Yesu adati, “Zimene ndimaphunzitsa si zangatu ai, ndi za Atate amene adandituma.
Yoh. 7:16ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
7
Yoh. 7:7
Anthu ongokonda zapansipano sangadane nanu, koma amadana ndi Ine, chifukwa ndimapereka umboni wosonyeza kuti ntchito zao nzoipa.
Yoh. 7:7ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
ပင်မစာမျက်နှာ
သမ္မာကျမ်းစာ
အစီအစဉ်များ
ဗီဒီယိုများ