1
Gen. 10:8
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Kusi adabereka Nimirodi. Nimirodi anali wankhondo woyamba wanyonga pa dziko lapansi.
နှိုင်းယှဉ်
Gen. 10:8ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
2
Gen. 10:9
Iyeyu analinso mlenje wamkulu pamaso pa Chauta. Nchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo chakuti, “Ndiwe mlenje wamkulu pamaso pa Chauta, ngati Nimirodi.”
Gen. 10:9ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
ပင်မစာမျက်နှာ
ကျမ်းစာ
အစီအစဉ်
ဗီဒီယို