1
YOHANE 5:24
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Indetu, indetu, ndinena kwa inu, kuti iye wakumva mau anga, ndi kukhulupirira Iye amene anandituma Ine, ali nao moyo wosatha, ndipo salowa m'kuweruza, koma wachokera kuimfa, nalowa m'moyo.
Bandingkan
Selidiki YOHANE 5:24
2
YOHANE 5:6
Yesu, pakuona ameneyo alikugona, ndipo anadziwa kuti anatero nthawi yaikulu pamenepo, ananena naye, Ufuna kuchiritsidwa kodi?
Selidiki YOHANE 5:6
3
YOHANE 5:39-40
Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo; ndipo simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo.
Selidiki YOHANE 5:39-40
4
YOHANE 5:8-9
Yesu ananena naye, Tauka, yalula mphasa yako, nuyende. Ndipo pomwepo munthuyu anachira, nayalula mphasa yake, nayenda. Koma tsiku lomwelo linali la Sabata.
Selidiki YOHANE 5:8-9
5
YOHANE 5:19
Pamenepo Yesu anayankha nati kwa iwo, Indetu, indetu ndinena kwa inu, sakhoza Mwana kuchita kanthu pa yekha, koma chimene aona Atate achichita, ndicho. Pakuti zimene Iye azichita, zomwezo Mwananso azichita momwemo.
Selidiki YOHANE 5:19
Halaman Utama
Alkitab
Pelan
Video