Logo YouVersion
AlkitabPelanVideo
Dapatkan apl
Pemilih Bahasa
Ikon Carian

Ayat Alkitab yang Popular daripada YOHANE 2

1

YOHANE 2:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita m'Kana wa m'Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

Bandingkan

Selidiki YOHANE 2:11

2

YOHANE 2:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

Bandingkan

Selidiki YOHANE 2:4

3

YOHANE 2:7-8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

Bandingkan

Selidiki YOHANE 2:7-8

4

YOHANE 2:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

Bandingkan

Selidiki YOHANE 2:19

5

YOHANE 2:15-16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse m'Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

Bandingkan

Selidiki YOHANE 2:15-16

Bab Sebelumnya
Bab Seterusnya
YouVersion

Mendorong dan mencabar anda untuk mencari hubungan rapat dengan Allah setiap hari.

Pelayanan

Perihal

Kerjaya

Jadi Sukarelawan

Blog

Akhbar

Pautan Berguna

Bantuan

Menderma

Versi Alkitab

Alkitab Audio

Bahasa Alkitab

Ayat Hari Ini


Pelayanan Digital

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Polisi PrivasiTerma
Program Pendedahan Kerentanan
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Halaman Utama

Alkitab

Pelan

Video