Logo YouVersion
AlkitabPelanVideo
Dapatkan apl
Pemilih Bahasa
Ikon Carian

Ayat Alkitab yang Popular daripada LUKA 19

1

LUKA 19:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.

Bandingkan

Selidiki LUKA 19:10

2

LUKA 19:38

Buku Lopatulika

BLP-2018

nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere mu Mwamba, ndi ulemerero mu Mwambamwamba.

Bandingkan

Selidiki LUKA 19:38

3

LUKA 19:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu.

Bandingkan

Selidiki LUKA 19:9

4

LUKA 19:5-6

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo m'mene anadza pamalopo Yesu anakweza maso nati kwa iye, Zakeyo, fulumira, nutsike; pakuti lero ndiyenera kukhala m'nyumba mwako. Ndipo anafulumira, natsika, namlandira Iye wokondwera.

Bandingkan

Selidiki LUKA 19:5-6

5

LUKA 19:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Zakeyo anaimirira nati kwa Ambuye, Taonani, Ambuye, gawo limodzi la zanga zonse zogawika pakati ndipatsa osauka; ndipo ngati ndalanda kanthu kwa munthu monyenga, ndimbwezera kanai.

Bandingkan

Selidiki LUKA 19:8

6

LUKA 19:39-40

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

Bandingkan

Selidiki LUKA 19:39-40

Pelan Bacaan dan Renungan percuma yang berkaitan dengan LUKA 19

Bab Sebelumnya
Bab Seterusnya
YouVersion

Mendorong dan mencabar anda untuk mencari hubungan rapat dengan Allah setiap hari.

Pelayanan

Perihal

Kerjaya

Jadi Sukarelawan

Blog

Akhbar

Pautan Berguna

Bantuan

Menderma

Versi Alkitab

Alkitab Audio

Bahasa Alkitab

Ayat Hari Ini


Pelayanan Digital

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Polisi PrivasiTerma
Program Pendedahan Kerentanan
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Halaman Utama

Alkitab

Pelan

Video