1
YOHANE 7:38
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake.
Харьцуулах
YOHANE 7:38 г судлах
2
YOHANE 7:37
Koma tsiku lomaliza, lalikululo la chikondwerero, Yesu anaimirira nafuula, ndi kunena, Ngati pali munthu akumva ludzu, adze kwa Ine, namwe.
YOHANE 7:37 г судлах
3
YOHANE 7:39
Koma ichi anati za Mzimu, amene iwo akukhulupirira Iye anati adzalandire; pakuti Mzimu panalibe pamenepo, chifukwa Yesu sanalemekezedwe panthawi pomwepo.
YOHANE 7:39 г судлах
4
YOHANE 7:24
Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.
YOHANE 7:24 г судлах
5
YOHANE 7:18
Iye wolankhula zochokera kwa iye yekha afuna ulemu wa mwini yekha. Iye wakufuna ulemu wa Iye amene anamtuma, yemweyu ali woona, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama.
YOHANE 7:18 г судлах
6
YOHANE 7:16
Pamenepo Yesu anayankha iwo, nati, Chiphunzitso changa sichili changa, koma cha Iye amene anandituma Ine.
YOHANE 7:16 г судлах
7
YOHANE 7:7
Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa.
YOHANE 7:7 г судлах
Нүүр хуудас
Библи
Тѳлѳвлѳгѳѳ
Видео