1
Yoh. 5:24
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
“Ndithu ndikunenetsa kuti munthu womva mau anga, nakhulupirira Iye amene adandituma, ameneyo ali ndi moyo wosatha. Iyeyo sazengedwa mlandu, koma watuluka kale mu imfa, ndipo waloŵa m'moyo.
Salīdzināt
Izpēti Yoh. 5:24
2
Yoh. 5:6
Yesu adamuwona ali gone, nadziŵa kuti adaadwala nthaŵi yaitali. Tsono adamufunsa kuti, “Kodi ukufuna kuchira?”
Izpēti Yoh. 5:6
3
Yoh. 5:39-40
Mumaphunzira Malembo mozama, chifukwa mumaganiza kuti mupezamo moyo wosatha. Ndipotu ndi Malembo omwewo amene akundichitira umboni! Komabe inu simufuna kudza kwa Ine kuti mukhale ndi moyo.
Izpēti Yoh. 5:39-40
4
Yoh. 5:8-9
Yesu adamlamula kuti, “Dzuka, tenga mphasa yako, yamba kuyenda.” Pompo munthuyo adachiradi, nanyamula mphasa yake nkuyamba kuyenda. Tsikulo linali la Sabata.
Izpēti Yoh. 5:8-9
5
Yoh. 5:19
Tsono Yesu adati, “Kunena zoona Ine Mwanane sindingathe kuchita kanthu pandekha. Ndimangochita zimene ndikuwona Atate anga akuchita. Zimene Atate amachita, Mwana amachitanso zomwezo.
Izpēti Yoh. 5:19
Mājas
Bībele
Plāni
Video