1
LUKA 10:19
Buku Lopatulika
Taonani, ndakupatsani ulamuliro wakuponda pa njoka ndi zinkhanira, ndi pa mphamvu iliyonse ya mdaniyo; ndipo kulibe kanthu kadzakuipsani konse.
Salīdzināt
Izpēti LUKA 10:19
2
LUKA 10:41-42
Koma Ambuye anayankha nati kwa iye, Marita, Marita, uda nkhawa nuvutika ndi zinthu zambiri; koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye.
Izpēti LUKA 10:41-42
3
LUKA 10:27
Ndipo iye anayankha nati, Uzikonda Ambuye Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mphamvu yako yonse, ndi nzeru zako zonse, ndi mnansi wako monga iwe mwini.
Izpēti LUKA 10:27
4
LUKA 10:2
Ndipo ananena kwa iwo, Dzinthu dzichuluka, koma antchito achepa; potero pemphani Mwini dzinthu, kuti akankhe antchito kukututa kwake.
Izpēti LUKA 10:2
5
LUKA 10:36-37
Uti wa awa atatu, uyesa iwe, anakhala mnansi wa iye uja adagwa m'manja a achifwamba? Ndipo anati, Iye wakumchitira chifundo. Ndipo Yesu anati kwa iye, Pita nuchite iwe momwemo.
Izpēti LUKA 10:36-37
6
LUKA 10:3
Mukani; taonani, Ine ndituma inu ngati anaankhosa pakati pa mimbulu.
Izpēti LUKA 10:3
Mājas
Bībele
Plāni
Video