„YouVersion“ logotipas
BiblijaPlanaiVaizdo įrašai
Gaukite programėlę
Kalbos parinkiklis
Paieškos piktograma

Populiarios Biblijos eilutės iš GENESIS 4

1

GENESIS 4:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ukachita zabwino, sudzalandiridwa kodi? Ukaleka kuchita zabwino, uchimo ubwatama pakhomo: kwa iwe kudzakhala kulakalaka kwake, ndipo iwe udzamlamulira iye.

Palyginti

Naršyti GENESIS 4:7

2

GENESIS 4:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.

Palyginti

Naršyti GENESIS 4:26

3

GENESIS 4:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?

Palyginti

Naršyti GENESIS 4:9

4

GENESIS 4:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati, Wachita chiyani? Mau a mwazi wa mphwako andifuulira Ine kunthaka.

Palyginti

Naršyti GENESIS 4:10

5

GENESIS 4:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.

Palyginti

Naršyti GENESIS 4:15

Ankstesnis skyrius
Kitas skyrius
„YouVersion“

Skatina ir kviečia jus kasdieną ieškoti artumo su Dievu.

Tarnystė

Apie

Karjera

Savanoriaukite

Tinklaraštis

Spaudai

Naudingos nuorodos

Pagalba

Paaukokite

Biblijos versijos

Įgarsintos Biblijos

Biblijos kalbos

Dienos eilutė


Skaitmeninė tarnystė, kurią vykdo

Life.Church
English (US)

©2025 „Life.Church“ / „YouVersion“

Privatumo politikaSąlygos
Pažeidžiamumų atskleidimo programa
„Facebook“„Twitter“„Instagram“„YouTube“„Pinterest“

Pradžia

Biblija

Planai

Vaizdo įrašai