Gen. 22:15-16

Gen. 22:15-16 BLY-DC

Mngelo wa Chauta uja adamuitana Abrahamu kachiŵiri kuchokera kumwamba, adati, “Chauta akunena kuti, ‘Ndikulumbira kuti ndidzakudalitsa kwambiri iwe chifukwa wachita zimenezi, osandimana mwana wako mmodzi yekha uja.

Gen. 22 ಓದಿ