1
Gen. 25:23
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Chauta adamuuza kuti, “M'mimba mwako muli mitundu iŵiri ya anthu. Udzabereka mafuko a anthu olimbana: mwana wina adzakhala wamphamvu kupambana mnzake, wamkulu adzakhala wotumikira wamng'ono.”
ತಾಳೆಮಾಡಿ
Gen. 25:23 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
Gen. 25:30
Anali ndi njala zedi, motero adauza Yakobe kuti, “Ine njala yandipha. Patseko nyemba zofiira waphikazi.” (Nchifukwa chake adamutcha Edomu.)
Gen. 25:30 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
Gen. 25:21
Tsono poti mkazi wa Isaki anali wosabereka, Isakiyo adapempherera mkazi wake kwa Chauta. Chauta adamva pemphero lake, ndipo Rebeka adatenga pathupi.
Gen. 25:21 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
Gen. 25:32-33
Esau adati, “Chabwino, inetu ndili pafupi kufa. Kodi ukulu wangawo udzandipinduliranji?” Yakobe adati, “Uyambe walumbira kuti ukulu wakowo wandipatsadi.” Apo Esau adalumbira, nagulitsa ukulu wake wauchisamba kwa Yakobe.
Gen. 25:32-33 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
5
Gen. 25:26
Pobadwa mng'ono wake, dzanja lake linali litagwira chidendene cha Esau. Motero adamutcha Yakobe. Pamene ana ameneŵa ankabadwa, nkuti Isaki ali wa zaka 60.
Gen. 25:26 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
6
Gen. 25:28
Tsono Isaki ankakonda Esau chifukwa ankadya nyama imene Esauyo ankamupatsa akapha. Koma Rebeka ankakonda Yakobe.
Gen. 25:28 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
ಮುಖಪುಟ
ಬೈಬಲ್
ಯೋಜನೆಗಳು
ವೀಡಿಯೊಗಳು