1
Genesis 15:6
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Abramu anakhulupirira Yehova, ndipo ichi chinamuchititsa kukhala wolungama.
ತಾಳೆಮಾಡಿ
Genesis 15:6 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
Genesis 15:1
Zitatha izi, Yehova anayankhula ndi Abramu mʼmasomphenya nati: “Usaope Abramu. Ine ndili ngati chishango chokutchinjiriza. Mphotho yako idzakhala yayikulu.”
Genesis 15:1 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
Genesis 15:5
Yehova anapita naye Abramu panja nati, “Tayangʼana kumwambaku, ndipo chifukwa cha chimenechi uwerenge nyenyezi ngati ungathe kuziwerenga.” Ndipo anamuwuza kuti, “Ndi mmene adzakhalire ana ako ndi zidzukulu zako.”
Genesis 15:5 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
Genesis 15:4
Yehova anayankhula naye nati: “Munthu uyu sadzalowa mʼmalo mwako, koma mwana wako weniweni wamwamuna, wobereka wekha ndiye adzalowe mʼmalo mwako.”
Genesis 15:4 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
5
Genesis 15:13
Tsono Yehova anati kwa iye, “Uyenera kudziwa mosakayika kuti zidzukulu zako zidzakhala alendo mʼdziko lachilendo ndipo zidzakhala akapolo ndi kuzunzidwa zaka 400.
Genesis 15:13 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
6
Genesis 15:2
Koma Abramu anati, “Haa! Ambuye Yehova, mukhoza kundipatsa chiyani popeza ndikanali wopanda mwana ndipo amene adzatenge chuma changa ndi Eliezara wa ku Damasiko?
Genesis 15:2 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
7
Genesis 15:18
Pa tsiku limenelo, Yehova anachita pangano ndi Abramu nati, “Ndikulonjeza kuti ndidzapereka dziko ili kwa zidzukulu zako, kuchokera ku mtsinje wa ku Igupto mpaka ku mtsinje waukulu wa Yufurate.
Genesis 15:18 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
8
Genesis 15:16
Patapita mibado inayi, adzukulu ako adzabwereranso kuno popeza tchimo la Aamori silinafike pachimake kuti alangidwe.”
Genesis 15:16 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
ಮುಖಪುಟ
ಬೈಬಲ್
ಯೋಜನೆಗಳು
ವೀಡಿಯೊಗಳು