1
LUKA 22:42
Buku Lopatulika
nati, Atate, mukafuna Inu, chotsani chikho ichi pa Ine; koma si kufuna kwanga ai, komatu kwanu kuchitike.
ತಾಳೆಮಾಡಿ
LUKA 22:42 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
LUKA 22:32
koma ndinakupempherera kuti chikhulupiriro chako chingazime; ndipo iwe, pamene watembenuka ukhazikitse abale ako.
LUKA 22:32 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
LUKA 22:19
Ndipo m'mene adatenga mkate, nayamika, anaunyema, nawapatsa, nanena, Ichi ndi thupi langa lopatsidwa chifukwa cha inu; chitani ichi chikumbukiro changa.
LUKA 22:19 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
LUKA 22:20
Ndipo choteronso chikho, atatha mgonero, nanena, Chikho ichi ndi pangano latsopano m'mwazi wanga wothiridwa chifukwa cha inu.
LUKA 22:20 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
5
LUKA 22:44
Ndipo pokhala Iye m'chipsinjo mtima anapemphera kolimba koposa ndithu: ndi thukuta lake linakhala ngati madontho aakulu a mwazi alinkugwa pansi.
LUKA 22:44 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
6
LUKA 22:26
Koma sipadzatero ndi inu; komatu iye ali wamkulu mwa inu, akhale ngati wamng'ono; ndi iye ali woyamba, akhale ngati wotumikira.
LUKA 22:26 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
7
LUKA 22:34
Ndipo Iye anati, Ndikuuza iwe, Petro, sadzalira tambala lero lino kufikira udzakana katatu kuti sundidziwa Ine.
LUKA 22:34 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
ಮುಖಪುಟ
ಬೈಬಲ್
ಯೋಜನೆಗಳು
ವೀಡಿಯೊಗಳು