1
GENESIS 4:7
Buku Lopatulika
Ukachita zabwino, sudzalandiridwa kodi? Ukaleka kuchita zabwino, uchimo ubwatama pakhomo: kwa iwe kudzakhala kulakalaka kwake, ndipo iwe udzamlamulira iye.
ತಾಳೆಮಾಡಿ
GENESIS 4:7 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
GENESIS 4:26
Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.
GENESIS 4:26 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
GENESIS 4:9
Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?
GENESIS 4:9 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
GENESIS 4:10
Ndipo anati, Wachita chiyani? Mau a mwazi wa mphwako andifuulira Ine kunthaka.
GENESIS 4:10 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
5
GENESIS 4:15
Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.
GENESIS 4:15 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
ಮುಖಪುಟ
ಬೈಬಲ್
ಯೋಜನೆಗಳು
ವೀಡಿಯೊಗಳು