1
GENESIS 2:24
Buku Lopatulika
Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.
ತಾಳೆಮಾಡಿ
GENESIS 2:24 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
2
GENESIS 2:18
Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.
GENESIS 2:18 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
3
GENESIS 2:7
Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.
GENESIS 2:7 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
4
GENESIS 2:23
Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.
GENESIS 2:23 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
5
GENESIS 2:3
Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.
GENESIS 2:3 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
6
GENESIS 2:25
Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.
GENESIS 2:25 ಅನ್ವೇಷಿಸಿ
ಮುಖಪುಟ
ಬೈಬಲ್
ಯೋಜನೆಗಳು
ವೀಡಿಯೊಗಳು