1
Marko 8:35
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Pakuti aliyense amene afuna kupulumutsa moyo wake adzawutaya, koma aliyense amene ataya moyo wake chifukwa cha Ine ndi cha Uthenga Wabwino, adzawupulumutsa.
ប្រៀបធៀប
រុករក Marko 8:35
2
Marko 8:36
Kodi munthu adzapindulanji akalandira dziko lonse lapansi, koma ndi kutaya moyo wake?
រុករក Marko 8:36
3
Marko 8:34
Kenaka anayitana gulu la anthu pamodzi ndi ophunzira ake nati: “Ngati wina aliyense afuna kunditsata Ine, ayenera kudzikana yekha ndi kunyamula mtanda wake ndi kunditsata.
រុករក Marko 8:34
4
Marko 8:37-38
Kapena nʼchiyani chomwe munthu angapereke chosinthana ndi moyo wake? Ngati wina achita manyazi chifukwa cha Ine ndi mawu anga mu mʼbado uno wachigololo ndi wochimwa, Mwana wa Munthu adzachita naye manyazi pamene adzabwera mu ulemerero wa Atate ake pamodzi ndi angelo oyera.”
រុករក Marko 8:37-38
5
Marko 8:29
Iye anafunsa kuti, “Koma nanga inu, mumati ndine yani?” Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu.”
រុករក Marko 8:29
ទំព័រដើម
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ