1
Luka 2:11
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Lero mʼmudzi wa Davide wakubwadwirani Mpulumutsi; Iye ndi Khristu Ambuye.
ប្រៀបធៀប
រុករក Luka 2:11
2
Luka 2:10
Koma mngeloyo anawawuza kuti, “Musachite mantha. Ine ndakubweretserani Uthenga Wabwino wachimwemwe chachikulu umene udzakhala wa anthu onse.
រុករក Luka 2:10
3
Luka 2:14
“Ulemerero kwa Mulungu mmwambamwamba, ndi mtendere kwa anthu pa dziko lapansi amene Iye akondwera nawo.”
រុករក Luka 2:14
4
Luka 2:52
Ndipo Yesu anakula mu nzeru, msinkhu ndi chisomo cha Mulungu ndi anthu.
រុករក Luka 2:52
5
Luka 2:12
Ichi chidzakhala chizindikiro kwa inu: mukapeza mwana wakhanda wokutidwa ndi nsalu atagona modyera ngʼombe.”
រុករក Luka 2:12
6
Luka 2:8-9
Ndipo kunali abusa amene amakhala ku dera lomwelo, kuyangʼanira ziweto zawo usiku. Mngelo wa Ambuye anaonekera kwa iwo ndipo ulemerero wa Ambuye unawala mowazungulira. Iwo anachita mantha.
រុករក Luka 2:8-9
ទំព័រដើម
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ