1
Yohane 8:12
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Yesu atayankhulanso kwa anthu, anati, “Ine ndine kuwunika kwa dziko lapansi. Aliyense amene anditsata Ine sadzayenda mu mdima, koma adzakhala ndi kuwala kotsogolera anthu ku moyo.”
ប្រៀបធៀប
រុករក Yohane 8:12
2
Yohane 8:32
Tsono mudzadziwa choonadi, ndipo choonadicho chidzakumasulani.”
រុករក Yohane 8:32
3
Yohane 8:31
Kwa Ayuda amene anamukhulupirira, Yesu anati, “Ngati inu mutsatira chiphunzitso changa, ndithu ndinu ophunzira anga.
រុករក Yohane 8:31
4
Yohane 8:36
Nʼchifukwa chake ngati Mwana adzakumasulani, mudzakhala mfulu ndithu.
រុករក Yohane 8:36
5
Yohane 8:7
Pamene iwo anapitirira kumufunsa, Iye anaweramuka ndipo anawawuza kuti, “Ngati wina wa inu alipo wopanda tchimo, ayambe iyeyo kumugenda ndi miyala mkaziyu.”
រុករក Yohane 8:7
6
Yohane 8:34
Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wochita tchimo ndi kapolo wa tchimolo.
រុករក Yohane 8:34
7
Yohane 8:10-11
Yesu anaweramuka ndipo anamufunsa iye kuti, “Akuluakulu aja ali kuti? Kodi palibe amene wakutsutsa?” Iye anati, “Ambuye, palibe ndi mmodzi yemwe.” “Inenso sindikukutsutsa iwe. Pita kuyambira tsopano usakachimwenso.”
រុករក Yohane 8:10-11
គេហ៍
ព្រះគម្ពីរ
គម្រោងអាន
វីដេអូ