YouVersion Logo
ბიბლიაგეგმებივიდეოები
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from GENESIS 4

1

GENESIS 4:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ukachita zabwino, sudzalandiridwa kodi? Ukaleka kuchita zabwino, uchimo ubwatama pakhomo: kwa iwe kudzakhala kulakalaka kwake, ndipo iwe udzamlamulira iye.

Compare

Explore GENESIS 4:7

2

GENESIS 4:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.

Compare

Explore GENESIS 4:26

3

GENESIS 4:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?

Compare

Explore GENESIS 4:9

4

GENESIS 4:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati, Wachita chiyani? Mau a mwazi wa mphwako andifuulira Ine kunthaka.

Compare

Explore GENESIS 4:10

5

GENESIS 4:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.

Compare

Explore GENESIS 4:15

Free Reading Plans and Devotionals related to GENESIS 4

Previous Chapter
Next Chapter
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

შესახებ

Careers

მოხალისე

Blog

Press

Useful Links

Help

დახმარება

Bible Versions

აუდიო ბიბლიები

Bible Languages

Verse of the Day


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

კონფიდენციალურობის წესდებაTerms
Vulnerability Disclosure Program
ფეისბუქიტვიტერზეინსტაგრამიYouTubePinterest

მთავარი

ბიბლია

გეგმები

ვიდეოები