YouVersion Logo
ბიბლიაგეგმებივიდეოები
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from GENESIS 2

1

GENESIS 2:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

Compare

Explore GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

Compare

Explore GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

Compare

Explore GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

Compare

Explore GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Buku Lopatulika

BLP-2018

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

Compare

Explore GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Buku Lopatulika

BLP-2018

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

Compare

Explore GENESIS 2:25

Free Reading Plans and Devotionals related to GENESIS 2

Previous Chapter
Next Chapter
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

შესახებ

Careers

მოხალისე

Blog

Press

Useful Links

Help

დახმარება

Bible Versions

აუდიო ბიბლიები

Bible Languages

Verse of the Day


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

კონფიდენციალურობის წესდებაTerms
Vulnerability Disclosure Program
ფეისბუქიტვიტერზეინსტაგრამიYouTubePinterest

მთავარი

ბიბლია

გეგმები

ვიდეოები