YouVersionロゴ
聖書読書プランビデオ
アプリを入手
言語選択
検索アイコン

Gen. 2の有名な聖句

1

Gen. 2:24

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.

比較

Gen. 2:24で検索

2

Gen. 2:18

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”

比較

Gen. 2:18で検索

3

Gen. 2:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.

比較

Gen. 2:7で検索

4

Gen. 2:23

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”

比較

Gen. 2:23で検索

5

Gen. 2:3

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.

比較

Gen. 2:3で検索

6

Gen. 2:25

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.

比較

Gen. 2:25で検索

前章
次章
YouVersion

日々、神との親しい交わりを求めるために、あなたを励まし、勇気を与えます。

ミニストリー

概要

キャリア

ボランティア

ブログ

プレス

便利なリンク集

ヘルプ

寄付

聖書の訳

オーディオ聖書

聖書の言語

今日の聖句


デジタルミニストリー

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

プライバシー規約利用規約
脆弱性の開示
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

ホーム

聖書

読書プラン

ビデオ