YouVersionロゴ
聖書読書プランビデオ
アプリを入手
言語選択
検索アイコン

GENESIS 4の有名な聖句

1

GENESIS 4:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ukachita zabwino, sudzalandiridwa kodi? Ukaleka kuchita zabwino, uchimo ubwatama pakhomo: kwa iwe kudzakhala kulakalaka kwake, ndipo iwe udzamlamulira iye.

比較

GENESIS 4:7で検索

2

GENESIS 4:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.

比較

GENESIS 4:26で検索

3

GENESIS 4:9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?

比較

GENESIS 4:9で検索

4

GENESIS 4:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati, Wachita chiyani? Mau a mwazi wa mphwako andifuulira Ine kunthaka.

比較

GENESIS 4:10で検索

5

GENESIS 4:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.

比較

GENESIS 4:15で検索

前章
次章
YouVersion

日々、神との親しい交わりを求めるために、あなたを励まし、勇気を与えます。

ミニストリー

概要

キャリア

ボランティア

ブログ

プレス

便利なリンク集

ヘルプ

寄付

聖書の訳

オーディオ聖書

聖書の言語

今日の聖句


デジタルミニストリー

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

プライバシー規約利用規約
脆弱性の開示
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

ホーム

聖書

読書プラン

ビデオ