YouVersionロゴ
聖書読書プランビデオ
アプリを入手
言語選択
検索アイコン

GENESIS 2の有名な聖句

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

比較

GENESIS 2:24で検索

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

比較

GENESIS 2:18で検索

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

比較

GENESIS 2:7で検索

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

比較

GENESIS 2:23で検索

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

比較

GENESIS 2:3で検索

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

比較

GENESIS 2:25で検索

前章
次章
YouVersion

日々、神との親しい交わりを求めるために、あなたを励まし、勇気を与えます。

ミニストリー

概要

キャリア

ボランティア

ブログ

プレス

便利なリンク集

ヘルプ

寄付

聖書の訳

オーディオ聖書

聖書の言語

今日の聖句


デジタルミニストリー

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

プライバシー規約利用規約
脆弱性の開示
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

ホーム

聖書

読書プラン

ビデオ