Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from LUKA 16

1

LUKA 16:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Iye amene akhulupirika m'chaching'onong'ono alinso wokhulupirika m'chachikulu; ndipo iye amene ali wosalungama m'chachikulu.

Bera saman

Njòttu LUKA 16:10

2

LUKA 16:13

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Palibe mnyamata wa m'nyumba akhoza kukhala kapolo wa ambuye awiri; pakuti kapena adzamuda wina, nadzakonda winayo; kapena adzatsata wina, nadzapeputsa winayo. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa Chuma.

Bera saman

Njòttu LUKA 16:13

3

LUKA 16:11-12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake ngati simunakhala okhulupirika m'chuma cha chosalungama, adzakhulupirira inu ndani ndi chuma choona? Ndipo ngati simunakhala okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni?

Bera saman

Njòttu LUKA 16:11-12

4

LUKA 16:31

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.

Bera saman

Njòttu LUKA 16:31

5

LUKA 16:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yense wakusudzula mkazi wake, nakwatira wina, achita chigololo; ndipo iye amene akwatira wosudzulidwayo, achita chigololo.

Bera saman

Njòttu LUKA 16:18

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast LUKA 16

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd