1
YOHANE 13:34-35
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake. Mwa ichi adzazindikira onse kuti muli ophunzira anga, ngati muli nacho chikondano wina ndi mnzake.
Bera saman
Njòttu YOHANE 13:34-35
2
YOHANE 13:14-15
Chifukwa chake, ngati Ine Ambuye ndi Mphunzitsi, ndasambitsa mapazi anu, inunso muyenera kusambitsana mapazi wina ndi mnzake. Pakuti ndakupatsani inu chitsanzo, kuti, monga Ine ndakuchitirani inu, inunso muchite.
Njòttu YOHANE 13:14-15
3
YOHANE 13:7
Yesu anayankha nati kwa iye, Chimene ndichita Ine suchidziwa tsopano; koma udzadziwa m'tsogolo mwake.
Njòttu YOHANE 13:7
4
YOHANE 13:16
Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake; kapena mtumwi sali wamkulu ndi womtuma iye.
Njòttu YOHANE 13:16
5
YOHANE 13:17
Ngati mudziwa izi, odala inu ngati muzichita.
Njòttu YOHANE 13:17
6
YOHANE 13:4-5
ananyamuka pamgonero, navula malaya ake; ndipo m'mene adatenga chopukutira, anadzimanga m'chuuno. Pomwepo anathira madzi m'nsambidwe, nayamba kusambitsa mapazi a ophunzira ake, ndi kuwapukuta ndi chopukutira, chimene anadzimanga nacho.
Njòttu YOHANE 13:4-5
Heim
Biblía
Áætlanir
Myndbönd