Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from YOHANE 2

1

YOHANE 2:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita mu Kana wa mu Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

Bera saman

Njòttu YOHANE 2:11

2

YOHANE 2:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

Bera saman

Njòttu YOHANE 2:4

3

YOHANE 2:7-8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

Bera saman

Njòttu YOHANE 2:7-8

4

YOHANE 2:19

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

Bera saman

Njòttu YOHANE 2:19

5

YOHANE 2:15-16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse mu Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

Bera saman

Njòttu YOHANE 2:15-16

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast YOHANE 2

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd