1
Yoh. 18:36
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Yesu adayankha kuti, “Ufumu wanga si wapansipano ai. Ufumu wanga ukadakhala wapansipano, bwenzi anyamata anga atamenya nkhondo kuti ndisaperekedwe kwa akulu a Ayuda. Komatu ai, ufumu wanga si wapansipano.”
Konpare
Eksplore Yoh. 18:36
2
Yoh. 18:11
Apo Yesu adauza Petro kuti, “Bwezera lupanga lako m'chimake. Kodi ukuti ndisamwe chikho cha masautso chimene Atate andipatsa?”
Eksplore Yoh. 18:11
Akèy
Bib
Plan yo
Videyo