Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan GENESIS 2

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

Konpare

Eksplore GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

Konpare

Eksplore GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

Konpare

Eksplore GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

Konpare

Eksplore GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

Konpare

Eksplore GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

Konpare

Eksplore GENESIS 2:25

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo