1
GENESIS 7:1
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.
तुलना
खोजें GENESIS 7:1
2
GENESIS 7:24
Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.
खोजें GENESIS 7:24
3
GENESIS 7:11
Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.
खोजें GENESIS 7:11
4
GENESIS 7:23
Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.
खोजें GENESIS 7:23
5
GENESIS 7:12
Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.
खोजें GENESIS 7:12
YouVersion आपके अनुभव को वैयक्तिकृत करने के लिए कुकीज़ का उपयोग करता है। हमारी वेबसाइट का उपयोग करके, आप हमारी गोपनीयता नीति में वर्णित कुकीज़ के हमारे उपयोग को स्वीकार करते हैं।
होम
बाइबिल
योजनाएँ
वीडियो