YouVersion का प्रतीक चिन्ह
बाइबिलयोजनाएँवीडियो
ऐप प्राप्त करें
भाषा चयनकर्ता
खोज चिह्न

GENESIS 14से लोकप्रिय बाइबिल छंद

1

GENESIS 14:20

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ayamikike Mulungu Wamkulukulu amene wapereka adani ako m'dzanja lako. Ndipo anampatsa iye limodzi la magawo khumi la zonse.

तुलना

खोजें GENESIS 14:20

2

GENESIS 14:18-19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Melkizedeki mfumu ya ku Salemu, anatuluka nao mkate ndi vinyo: iye ndiye wansembe wa Mulungu Wamkulukulu. Ndipo anamdalitsa iye, nati, Abramu adalitsike ndi Mulungu Wamkulukulu, mwini kumwamba ndi dziko lapansi

तुलना

खोजें GENESIS 14:18-19

3

GENESIS 14:22-23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Abramu anati kwa mfumu ya Sodomu, Dzanja langa ndamtukulira Yehova, Mulungu Wamkulukulu, mwini kumwamba ndi dziko lapansi kuti sindidzatenga ngakhale thonje ngakhale chingwe cha nsapato, ngakhale kanthu kalikonse kako, kuti unganene, Ndamlemeza Abramu

तुलना

खोजें GENESIS 14:22-23

पिछला अध्याय
अगला अध्याय
YouVersion

हर दिन परमेश्वर के साथ घनिष्ठता तलाशने के लिए आपको प्रोत्साहित और चुनौती देना।

मिनिस्ट्री

के विषय में

पेशा

स्वयंसेवक

ब्लॉग

प्रेस

उपयोगी लिंक

सहायता

योगदान

बाईबिल की अन्य संस्करणे

ऑडियो बाइबिल

बाइबिल भाषाएँ

आज का पद्य


एक डिजिटल मिनिस्ट्री, ये वाले से -

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

निजी नीतिशर्तें
भेद्यता प्रकटीकरण कार्यक्रम
फेसबुकट्विट्टरइंस्टाग्रामयूट्यूबपिंटरेस्ट

होम

बाइबिल

योजनाएँ

वीडियो