1
GENESIS 10:8
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Kusi anabala Nimirodi; ndipo iye anayamba kukhala wamphamvu pa dziko lapansi.
השווה
חקרו GENESIS 10:8
2
GENESIS 10:9
Iye ndiye mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova: chifukwa chake kunanenedwa, Monga Nimirodi mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova.
חקרו GENESIS 10:9
בית
כתבי הקודש
תכניות
קטעי וידאו