YouVersion Logo
Search Icon

LUKA 16:11-12

LUKA 16:11-12 BLP-2018

Chifukwa chake ngati simunakhale okhulupirika m'chuma cha chosalungama, adzakhulupirira inu ndani ndi chuma choona? Ndipo ngati simunakhale okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni?

Free Reading Plans and Devotionals related to LUKA 16:11-12