YouVersion-Logo
BibelLesepläneVideos
Hol dir die App!
Sprachauswahl
Suchsymbol

Beliebte Verse in GENESIS 19

1

GENESIS 19:26

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.

Vergleichen

Studiere GENESIS 19:26

2

GENESIS 19:16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Koma anachedwa; ndipo anthuwo anamgwira dzanja lake, ndi dzanja la mkazi wake ndi dzanja la ana ake aakazi awiri; chifukwa cha kumchitira chifundo Yehova; ndipo anamtulutsa iye, namuika kunja kwa mzinda.

Vergleichen

Studiere GENESIS 19:16

3

GENESIS 19:17

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.

Vergleichen

Studiere GENESIS 19:17

4

GENESIS 19:29

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo panali pamene Mulungu anaononga mizinda ya m'chigwa, Mulungu anakumbukira Abrahamu, natulutsa Loti pakati pa chionongeko, pamene anaononga mizinda m'mene anakhalamo Loti.

Vergleichen

Studiere GENESIS 19:29

Kostenlose Lesepläne und Andachten zum Thema GENESIS 19

Vorheriges Kapitel
Nächstes Kapitel
YouVersion

Die App ermutigt und fordert dich heraus, jeden Tag die Gemeinschaft mit Gott zu suchen.

Dienst

Über

Jobangebote

Ehrenamtlich helfen

Blog

Presse

Nützliche Links

Hilfe

Spenden

Bibelübersetzungen

Hörbibeln

Bibelsprachen

Vers des Tages


Ein digitaler Dienst von

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

DatenschutzrichtlinieAGB
Verfahren zur Offenlegung von Sicherheitslücken (VDP)
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hauptbildschirm

Bibel

Lesepläne

Videos