ইউভার্শন লোগো
বাইবেলপরিকল্পনাগুলোভিডিও
অ্যাপটি ডাউনলোড করুন
ভাষা নির্বাচক
সার্চ আইকন

Popular Bible Verses from YOHANE 2

1

YOHANE 2:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita mu Kana wa mu Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

তুলনা করুন

Explore YOHANE 2:11

2

YOHANE 2:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

তুলনা করুন

Explore YOHANE 2:4

3

YOHANE 2:7-8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

তুলনা করুন

Explore YOHANE 2:7-8

4

YOHANE 2:19

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

তুলনা করুন

Explore YOHANE 2:19

5

YOHANE 2:15-16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse mu Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

তুলনা করুন

Explore YOHANE 2:15-16

YOHANE 2 এর সাথে সম্পর্কিত বিনামূল্যের পাঠ পরিকল্পনা ও আরাধনা সহায়িকা

পূর্ববর্তী অধ্যায়
পরের অধ্যায়
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

সম্বন্ধে

Careers

স্বেচ্ছাসেবক

ব্লগ

প্রেস

Useful Links

সহায়তা

অনুদান দিন

বাইবেল সংস্করণ

অডিও বাইবেল

বাইবেলের ভাষা

আজকের আয়াত


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2026 Life.Church / YouVersion

গোপনীয়তার নীতিমালাশর্তাবলী
Vulnerability Disclosure Program
ফেসবুকটুইটারইনস্টাগ্রামইউটিউবPinterest