YouVersion Logo
Search Icon

Mal. 4:1

Mal. 4:1 BLY-DC

Chauta Wamphamvuzonse akunena kuti, “Tsiku likubwera pamene anthu onse odzikuza ndi ochita zoipa adzapsa ngati chiputu m'ng'anjo. Tsiku limenelo adzapserereratu osatsalako muzu kapena nthambi. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mal. 4:1