YouVersion Logo
Search Icon

Gen. 22:15-16

Gen. 22:15-16 BLY-DC

Mngelo wa Chauta uja adamuitana Abrahamu kachiŵiri kuchokera kumwamba, adati, “Chauta akunena kuti, ‘Ndikulumbira kuti ndidzakudalitsa kwambiri iwe chifukwa wachita zimenezi, osandimana mwana wako mmodzi yekha uja.

Free Reading Plans and Devotionals related to Gen. 22:15-16