Ntc. 19:11-12
Ntc. 19:11-12 BLY-DC
Mulungu adachita zozizwitsa kwambiri kudzera kwa Paulo. Anthu ankati akatenga zitambaya kapena nsalu zina zimene Paulo ankagwiritsa ntchito, nakaziika pa anthu odwala, odwalawo ankachira, ndipo mizimu yoipa inkatuluka mwa iwo.