YouVersion Logo
Search Icon

LUKA 17:1-2

LUKA 17:1-2 BLPB2014

Ndipo anati kwa ophunzira ake, Sikutheka kuti zolakwitsa zisadze; koma tsoka iye amene adza nazo. Kukolowekedwa mwala wamphero m'khosi mwake ndi kuponyedwa iye m'nyanja nkwapafupi, koma kulakwitsa mmodzi wa ang'ono awa nkwapatali.

Free Reading Plans and Devotionals related to LUKA 17:1-2