YouVersion Logo
Search Icon

Yohane 13:4-5

Yohane 13:4-5 CCL

anayimirira kuchoka pa chakudya navula zovala zake natenga nsalu yopukutira nadzimanga mʼchiwuno mwake. Atachita izi, anathira madzi mʼbeseni ndi kuyamba kusambitsa mapazi a ophunzira ake, ndi kuwapukuta ndi chopukutira chimene anachimanga mʼchiwuno mwake.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yohane 13:4-5