1
Ntc. 22:16
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Nanga tsono ukuchedweranji? Dzuka ndi kutama dzina lake mopemba, ubatizidwe ndi kusambitsidwa kuti machimo ako achoke.’ ”
Compare
Explore Ntc. 22:16
2
Ntc. 22:14
Tsono adandiwuza kuti, ‘Mulungu wa makolo athu adakusankha kuti udziŵe zimene Iye akufuna, uwone Wolungama uja, ndipo umve mau ake olankhula nawe.
Explore Ntc. 22:14
3
Ntc. 22:15
Pakuti udzamchitira umboni kwa anthu onse pa zimene waziwona ndi kuzimva.
Explore Ntc. 22:15
Home
Bible
Plans
Videos