1
Ntc. 10:34-35
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Petro adayamba kulankhula, adati, “Zoonadi ndazindikira tsopano kuti Mulungu alibe tsankho. Amalandira bwino munthu wa mtundu uliwonse womuwopa nkumachita chilungamo.
Compare
Explore Ntc. 10:34-35
2
Ntc. 10:43
Aneneri onse adamchitira umboni, ndi kunena kuti chifukwa cha dzina lake, Mulungu adzakhululukira machimo a munthu aliyense wokhulupirira Iyeyu.”
Explore Ntc. 10:43
Home
Bible
Plans
Videos