1
2 SAMUELE 9:7
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo Davide ananena naye, Usaopa, pakuti zoonadi ndidzakuchitira kukoma mtima chifukwa cha Yonatani atate wako; ndi minda yonse ya Saulo ndidzakubwezera, ndipo udzadya pa gome langa chikhalire.
Compare
Explore 2 SAMUELE 9:7
2
2 SAMUELE 9:1
Ndipo Davide anati, Kodi atsalako wina wa nyumba ya Saulo, kuti ndimchitire chifundo chifukwa cha Yonatani?
Explore 2 SAMUELE 9:1
Home
Bible
Plans
Videos