1
Masalimo 104:34
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Zolingalira zanga zikhale zomukomera Iye, pamene ndikusangalala mwa Yehova.
Compare
Explore Masalimo 104:34
2
Masalimo 104:33
Ine ndidzayimbira Yehova moyo wanga wonse; ndidzayimbira matamando Mulungu wanga nthawi yonse imene ndili ndi moyo.
Explore Masalimo 104:33
3
Masalimo 104:1
Tamanda Yehova, iwe moyo wanga. Inu Yehova Mulungu wanga, ndinu wamkulu kwambiri; mwavala ulemerero ndi ufumu.
Explore Masalimo 104:1
Home
Bible
Plans
Videos