1
MARKO 15:34
Buku Lopatulika
Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine?
Compare
Explore MARKO 15:34
2
MARKO 15:39
Ndipo pamene kenturiyo, woimirirapo popenyana ndi Iye, anaona kuti anapereka mzimu kotero, anati, Zoonadi, munthu uyu anali Mwana wa Mulungu.
Explore MARKO 15:39
3
MARKO 15:38
Ndipo chinsalu chotchinga cha mu Kachisi chinang'ambika pakati, kuyambira kumwamba kufikira pansi.
Explore MARKO 15:38
4
MARKO 15:37
Ndipo Yesu anatulutsa mau okweza, napereka mzimu wake.
Explore MARKO 15:37
5
MARKO 15:33
Ndipo pofika ora lachisanu ndi chimodzi, panali mdima padziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.
Explore MARKO 15:33
6
MARKO 15:15
Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.
Explore MARKO 15:15
Home
Bible
Plans
Videos